Nkhani Za M'maboma

Nkhani Za M'maboma

Share

🌍THIS IS THE LATEST & FASTEST GROWING PAGE FOR BREAKING NEWS🌏 . Welcome 😎kuing'alura osaopa😎πŸ’ͺπŸ’ͺ

10/04/2026

NKHANI YOMVETSA CHISONI KWAMBIRI πŸ˜­πŸ’”

Pa nseu wa nguludi odzera mminda ya kwa kamwana muboma la Dowa pa trade ya Mponera kwapezeka mai waphedwa alindi mwana kumbuyo imagine kumupha munthu wamayi mwana ali ku nsana πŸ˜­πŸ’”

Malemuyu anali ndi ID pali zina lokha ndilomwe likuwoneka bwino,zonse pa ID sizikuwoneka bwino bwino.

Zina la malemuwa ndi Ida kamumwamba.

Mwana wa amalemuwa Ali moyo .

Nkhani yik*t eni munda anatuma ana atchito k*t akatcholeko ndiwo kumunda,anyamatawa atafika kumunda anapeza mwana akulila mmunda momwemo. Atayang'ana anapeza pali mayi koma atafa kale mwana alimusi mwa chitandacho akulira.

Apa ndipo anyamata aja anapita kumuzi kukauza anthu zangoziyi.

kwawo kwa malemuwa sikuziwika

Pempho zinthuzi zachitika dzulo madzulo πŸ’”πŸ˜­

10/04/2026

Ngati ukava Dzina la
Mulungu limakubowa
Dusa
Usalembe AMEN πŸ™πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­πŸ˜­

07/02/2026

Ambuye adaliseni awa😭 Asitheni nyengo zawo Ngati akwanise kulemba amen ndikupanga gawa uthengawu kumagulu awoπŸ‘‰( MULUNGU NDI MATHERO AMAVUTO ONSE)

09/10/2025

Nkhan

Apolisi m'boma la Ntchisi atsimikiza za imfa ya mwana wa miyezi inayi, Alexander Chimpeni, wa m'mudzi mwa Chiwembu m'bomalo yemwe wamwalira mayi ake atamugwera pomwe amamenyana ndi munthu wina.

Malingana ndi m'neneri wa polisi m'bomali Salomy Zgambo wati patsikuli mayiyu amakangana ndi nzawo atamubeleka Alexander kunsana ndipo ali mkati mokangana ndewu inabuka pakati pa awiriwa ndipo mwatsoka mayiyu anagwa ndik*tsamila mwanayu.

Zgambo wati zitatero anathamangila naye ku chipatala cha Ntchisi komwe achipatala anatsimikiza k*ti mwanayu wamwalira.

Zotsatira za chipatala zawonetsa k*ti mwanayu wamwalira kaamba kovulala kwambiri m'mutu.

Wolemba: Maureen Kanyundo

09/10/2025

NKHAN YONGOTIPEZA KUMENE

Masewero apakati pa timu ya Malawi ndi Equatorial Guinea alepheleka kamba ka zifukwa zina.

Masewerowa amayenera kuchitika pa bwalo la Bingu National munzinda wa Lilongwe usiku wa lero.

Koma malinga ndi kalata ya bungwe la Fam, masewerowa alepheleka chifukwa timu ya Equatorial Guinea yalephera kufika m'dziko muno.

Tikupatsilani zambiri posachedwapa.

Wolemba Mabvuto Kambuwe

07/10/2025

Ndani ak*ti Kumwamba kwamukondera wadzuka ndi Moyo☝️

πŸ‘

30/09/2025

Ngati umakhulupilira k*ti Mulungu tsiku lina adzasintha nyengo za moyo wako
Tangolemba AMEN

Ndikugawa uthengawu kuma group atatu

27/09/2025

Shout out to my newest followers! Excited to have you onboard! Luke Nkhoma, Hendreson Banda, Felister Kapalamula, Tiyamike Lameck, Tamala Chaula, John Enock, Hannah Julius, Rombani Zulu, Chiku Wastaubi, Gomani Mw, Glady's Nikell Kabvina, Manzy Mwanyada, Washington Mtaghayo, George Mussah, Preciuos Jalison, Sailess Steve, Stephano Daniel, Rajji Chiyenda, Chenje Ethel, Julius Chionetsero Maulana Maulana, Phelisters Shemmah, Davie Makina, Dyson Innocent Chitwanga, Eliz Ndenda, Mathews Lozalio, KONDWAN CHINYAMA, Aubrey Ziwoya, Joseph Moyoh, Usu Dip Samu, Austin Mataya, Stephan Stephen, Anessa Mwangiwa, Lazalo Felix, Bles Mwale, Makwinja Kassim, Jefule Jefule, Mandala Chirwa, Maseko Phili, Danger Manyika, Watson Mwale, Mangwanje Mbewe, Promise Michael, Emran Balakas, Shafi Kassim, Pemphelo James

27/09/2025

ZINA UKAMVA πŸ™„πŸ’”πŸ’”πŸ’”πŸ’”

Anyamata awiri omwe pakadalipano sakudziwika mayina awo apezeka atafa mam'mawa uno pafupi ndi malo okwelera minibus zopita mu Limbe omwe ndi oyandikana ndi nyumba za Blantyre Water Board komwe ndi kuseli kwa Kamuzu Stadium.

Anthuwa omwe matupi awo akuoneka ndi zilonda komanso magazi akuganiziridwa k*ti achita chophedwa ndi anthu okwiya atagwidwa akuba zipangizo za khebo za lamya pamalo omwe ali pafupi ndi pamene afera pomwe paonetsa k*ti anali atayamba kale kudula ma khebowa potengera k*ti mmanja mwawo mukuonetsa atavala zozitetedzera (gloves) zomwe anavala munthawi yomwe amayamba kuchotsa zipangizozi.

22/09/2025

Ndikuona anthu 1000 on this page Mulungu ak*tembenuza nyengo zawo kukhala umboni wachimwemwe, mu dzina la Yesu ChristπŸ™πŸ•ŠοΈπŸ•ŠοΈ

Want your business to be the top-listed Beauty Salon in Lilongwe?
Click here to claim your Sponsored Listing.

Website

Address

Lilongwe
INVITESOTHERSTOLIKETHISPAGEOF