The Rez Nation TV
βlaugh till cryingβ ππ₯π
New page, support me guys.π²πΌπΏπ²πΏπ¦π²πΏ πΏπΌπ°πͺ
POV: You try to surprise your wife and she activates self-defense mode ππ₯
"Laugh π until crying"π
New page, support me guys π π
When you try to be the craver oneβ¦ but sheβs already ahead π
π₯
New page, support me guys π π
βWen you Married to a man who never takes anything serious ππ₯β
β laugh till crying ππ₯β
New page, support me guys ππ
When she finds cheating messages in your phoneβ¦ pray for yourself π
βOnly legends will laugh till crying ππ₯β
New page, support me guys ππ
21/03/2026
Breaking news π° π πΊ π₯
Anthu angapo omwe akukhala mβdziko la South Africa popanda mapepala ovomerezeka agwidwa ndi akuluakulu a boma pa nthawi ya chikondwerero cha Eid Mubarak.
Malinga ndi malipoti, anthuwo anapezeka ali pa msonkhano wokondwerera Eid, komwe akuluakulu a chitetezo ndi a za immigration anachita opareshoni yofufuza anthu osaloledwa kukhala mβdzikolo.
Zikudziwika kuti ena mwa anthu omwe agwidwawo ndi ochokera ku Malawi, ngakhale chiwerengero chenicheni sichinatchulidwe.
Akuluakulu akuti opareshoniyi ndi gawo la kuyesetsa kulimbikitsa malamulo okhudza kulowa ndi kukhala mβdziko, ndipo anthu omwe apezeka alibe zikalata akuyembekezeka kupita nawo ku malo osungiramo anthu osaloledwa asanabweretsedwe kumayiko awo.
Boma la South Africa likupitiriza kulimbikitsa anthu onse obwera kudziko lino kuti azitsatira malamulo ndi kukhala ndi zikalata zovomerezeka.
ENGLISH:π°π
Several undocumented immigrants were arrested in South Africa during an Eid Mubarak celebration.
Authorities conducted an operation at the gathering, where they discovered individuals without valid permits. Some of those arrested are reportedly from MALAWI.
Officials say the operation is part of ongoing efforts to enforce immigration laws.
21/03/2026
Breaking news π°ππΊ
Mkulu wakale wa MALAWI Immigration a Charles Kalumo aopseza bwalo lamilandu kuti ngati siliwapatsa bello ayambilanso kunyanyala chakudya.
Kalumo anamangidwa lachitatu akuchokela ku South Africa ndipo pano ali kuchipatala china mumzinda wa Lilongwe kumene akulandila thandizo moyang'anilidwa ndi apolisi.
ENGLISHπ°π
Former Malawi Immigration Chief Charles Kalumo has threatened the court that if he is not granted bail, he will resume his hunger strike.
Kalumo was arrested on Wednesday upon his return from South Africa and is currently admitted to a hospital in Lilongwe, where he is receiving treatment under police guard.
The Rez Nation TV
Eyes can lie π
this guy was pretending to be a womanβ¦uyu amubathaππ
βLaugh now, cry later π stay sharp!ππ₯β
New page, support me guys ππ
Zakazaka wampalamula mponda matikiπ ulemu wanu mr kamkudzukudzu Passover Channel With Zaka ππ
βOnly legends will laugh till crying ππ₯β
New page, support me guys ππ
βOnly legends will laugh till crying ππ₯β
New page, support me guys ππ
Imfa iweyoππ
21/03/2026
SAD NEWS ( South Africa )
Akasia, outside Pretoria; R566 Rama City behind Sefako Makgatho University.
Rocks are being placed on the road. Three people died after they crashed head-on into a truck
trying to avoid the rocks.
Ku Pretoria dera lotchedwa AKasia ku nsewu wa R566 kuseli kwa Sefako Makgatho University kwada anthu atatu omwe alipachithunzipa,
Malingana ndi malipoti akuti anthu osadziwika bwino akumaika miyala pa nsewu kuti odutsa ndi magalimoto azigwa moti anthu atatuwa amwalira pomwe amazemba miyala yo galimoto zawo zinagudubuka ataombana ndi truck pomwe amayesera kuzemba miyala
The Rez Nation TV πΊ
21/03/2026
NKHANI ZOPATSA CHIDWIπ’π
Zigawenga ziwiri zapasidwa chilango chokakhala ku ndebe moyo wonse, chifukwa chopha mkazi wa zaka 21 yemwe anali ndi pakati (miyezi 8). Mumzinda wa Cape Town
Mayi, Shahieda Nathan, aphedwa kutsatila pakyombera komwe kunachitika, koma zigawengazi zinati sanali cholinga chenicheni chopha mayiwo anangokhala munthu wolakwika pamalo olakwika.
Izi zikutanthauza kuti zigawengazo zinkafuna munthu wina, koma zinatha kuwombera ndi kupha mayiyo mwangozi.
Khoti lalikulu la ku Western Cape linaweruza anthu awiriwa (Jeremiah Fortuin ndi Ricardo Cloete) chilango cha moyo wonse chifukwa cha kupha koopsa kumeneku
The Rez Nation TV πΊ.
